Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 144:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Tambasulani manja anu kuchokera kumwamba.+

      Ndimasuleni ndi kundilanditsa m’madzi ambiri.+

      Mundilanditse m’manja mwa anthu achilendo,+

  • Maliro 3:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Madzi asefukira ndi kumiza mutu wanga,+ moti ndanena kuti: “Ndifa basi!”+

  • Yona 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndinatsala pang’ono kufa+ chifukwa madzi anandimiza.

      Zomera zam’nyanja zinakulunga mutu wanga.

  • Chivumbulutso 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako njokayo inalavula madzi+ ngati mtsinje kuchokera m’kamwa mwake, kulavulira mkazi uja, kuti amizidwe ndi mtsinjewo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena