Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Nthawi yomweyo Mose anatambasula dzanja lake ndi kuloza panyanja, ndipo nyanjayo inayamba kubwerera m’malo mwake, kuli pafupi kucha. Pamenepo Aiguputo anayamba kuthawa kuti madziwo asawapeze, koma Yehova anakutumulira Aiguputowo pakatikati pa nyanja.+

  • Ekisodo 15:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mwapemerera mpweya wanu,+ ndipo nyanja yawamiza.+

      Amira ngati mtovu m’madzi akuya.+

  • Salimo 136:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Amenenso anakutumulira Farao ndi gulu lake lankhondo m’Nyanja Yofiira:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena