Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 110:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Yehova walumbira+ (ndipo sadzasintha maganizo). Iye wati:+

      “Iwe ndiwe wansembe mpaka kalekale,+

      Monga mwa unsembe wa Melekizedeki!”+

  • Amosi 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, walumbira mwa kuyera kwake+ kuti, ‘“Taonani! Masiku adzafika pamene mudzanyamulidwa ndi ngowe zokolera nyama ndipo otsala anu adzawakola ndi mbedza za nsomba.+

  • Aheberi 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mofanana ndi zimenezi, Mulungu pofuna kuwatsimikizira kwambiri anthu olandira lonjezolo monga cholowa chawo,+ kuti chifuniro chake n’chosasinthika,+ anachita kulumbira pa zimene analonjezazo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena