Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Yehova amawombola moyo wa atumiki ake.+

      Ndipo palibe aliyense wothawira kwa iye amene adzapezeka wolakwa.+

  • Salimo 56:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti inu mwalanditsa moyo wanga ku imfa.+

      Inu mwateteza phazi langa kuti lisapunthwe,+

      Kuti ndiyendeyende pamaso pa Mulungu m’kuwala kumene kumaunikira anthu amoyo.+

  • Salimo 69:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yandikirani moyo wanga ndi kuupulumutsa.+

      Ndiwomboleni kwa adani anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena