Salimo 17:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Mapazi anga ayendebe m’njira zanu,+Mmene sadzapunthwa ngakhale pang’ono.+ Salimo 94:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Pamene ndinanena kuti: “Phazi langa literereka,”+Kukoma mtima kwanu kosatha, inu Yehova, kunandichirikiza.+
18 Pamene ndinanena kuti: “Phazi langa literereka,”+Kukoma mtima kwanu kosatha, inu Yehova, kunandichirikiza.+