-
Salimo 78:42Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
42 Iwo sanakumbukire dzanja la Mulungu,+
Sanakumbukire tsiku limene anawawombola kwa mdani wawo,+
-
Yesaya 63:7Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
7 Ndidzanena za ntchito za Yehova zosonyeza kukoma mtima kwake kosatha.+ Ndidzatamanda Yehova, mogwirizana ndi zonse zimene Yehova watichitira.+ Ndidzauza nyumba ya Isiraeli zabwino zochuluka+ zimene iye wawachitira chifukwa cha chifundo chake,+ komanso chifukwa cha kukoma mtima kwake kosatha ndiponso kwakukulu.
-
-
-