Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 31:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 “Tsopano dzilembereni nyimbo iyi+ ndi kuwaphunzitsa ana a Isiraeli.+ Muiike m’kamwa mwawo kuti nyimbo imeneyi ikhale mboni yanga pamaso pa ana a Isiraeliwo.+

  • Yoswa 4:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Muzidzawauza kuti, ‘N’chifukwa chakuti madzi a mumtsinje wa Yorodano anadukana pamaso pa likasa la pangano la Yehova.+ Likasalo litadutsa mumtsinje wa Yorodano, madzi a mtsinje wa Yorodanowo anadukana, ndipo miyala imeneyi ndi chikumbutso cha zimenezo kwa ana a Isiraeli mpaka kalekale.’”*+

  • Salimo 102:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma inu Yehova, mudzakhalapobe kwamuyaya,+

      Dzina lanu* lidzakhalapobe ku mibadwomibadwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena