Deuteronomo 4:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 “Koma khalani tcheru ndipo musamale moyo wanu,+ kuti musaiwale zinthu zimene maso anu anaona,+ ndi kuti mitima yanu isaiwale zinthu zimenezo masiku onse a moyo wanu.+ Ana anu ndi zidzukulu zanu muziwauza za zinthu zimenezo,+ Deuteronomo 11:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Ana anu muwaphunzitsenso mawu amenewa, ndipo muzilankhula nawo za mawuwa mukakhala pansi m’nyumba mwanu, poyenda pamsewu, pogona ndi podzuka.+
9 “Koma khalani tcheru ndipo musamale moyo wanu,+ kuti musaiwale zinthu zimene maso anu anaona,+ ndi kuti mitima yanu isaiwale zinthu zimenezo masiku onse a moyo wanu.+ Ana anu ndi zidzukulu zanu muziwauza za zinthu zimenezo,+
19 Ana anu muwaphunzitsenso mawu amenewa, ndipo muzilankhula nawo za mawuwa mukakhala pansi m’nyumba mwanu, poyenda pamsewu, pogona ndi podzuka.+