Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Koma khalani tcheru ndipo musamale moyo wanu,+ kuti musaiwale zinthu zimene maso anu anaona,+ ndi kuti mitima yanu isaiwale zinthu zimenezo masiku onse a moyo wanu.+ Ana anu ndi zidzukulu zanu muziwauza za zinthu zimenezo,+

  • Deuteronomo 6:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 ndi kuwakhomereza mwa ana ako.+ Uzilankhula nawo za mawuwo ukakhala pansi m’nyumba mwako, poyenda pamsewu, pogona+ ndi podzuka.

  • Salimo 34:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Bwerani kuno ana anga, ndimvetsereni.+

      Ndikuphunzitsani kuopa Yehova.+

  • Salimo 78:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu anaika chikumbutso pakati pa ana a Yakobo,+

      Iye anaika chilamulo mu Isiraeli,+

      Zinthu zimene analamula makolo athu,+

      Kuti auze ana awo.+

  • Miyambo 22:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Phunzitsa mwana m’njira yomuyenerera.+ Ngakhale akadzakalamba sadzapatukamo.+

  • Aefeso 6:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Inunso abambo, musamapsetse mtima ana anu,+ koma muwalere+ m’malangizo*+ a Yehova* ndi kuwaphunzitsa kaganizidwe+ kake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena