Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 15:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Pamenepo iye anakhulupirira mwa Yehova,+ ndipo Mulunguyo anamuona Abulamu ngati wolungama.+

  • 2 Akorinto 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tsopano, popeza tili ndi mtima wachikhulupiriro wofanana ndi umene anaunena kuti: “Ndinali ndi chikhulupiriro, chotero ndinalankhula,”+ ifenso tili ndi chikhulupiriro, chotero tikulankhula,

  • Aheberi 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Chikhulupiriro+ ndicho chiyembekezo chotsimikizika cha zinthu zoyembekezeredwa,+ umboni wooneka wa zinthu zenizeni, ngakhale kuti n’zosaoneka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena