Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 23:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Sindisiya malamulo otuluka pakamwa pake.+

      Ndasunga mosamala mawu a pakamwa pake+ kuposa zimene akufuna kuti ndichite.

  • Salimo 119:174
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 174 Ndikulakalaka chipulumutso chanu, inu Yehova,+

      Ndipo ndimakonda kwambiri chilamulo chanu.+

  • Aroma 7:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mumtima mwanga+ ndimasangalala kwambiri+ ndi chilamulo cha Mulungu,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena