Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 49:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndithu ndidzayembekezera chipulumutso kwa inu, Yehova.+

  • 2 Samueli 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kodi si mmene nyumba yanga ilili kwa Mulungu?+

      Chifukwa chakuti anachita nane pangano lomwe lidzakhalapo mpaka kalekale,+

      Analikonza bwino ndipo n’lotetezeka.+

      Chifukwa ndilo chipulumutso changa+ ndi chondikondweretsa,

      Kodi chimenechi sindicho chifukwa chake adzakulitsa panganoli?+

  • Salimo 119:81
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  81 Ine ndafooka chifukwa cholakalaka chipulumutso chanu,+

      Pakuti ndayembekezera mawu anu.+

  • Chivumbulutso 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iwo anapitirizabe kufuula ndi mawu okweza, kuti: “Chipulumutso chathu chachokera kwa Mulungu wathu,+ amene wakhala pampando wachifumu,+ ndi kwa Mwanawankhosa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena