Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 22:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Yehova akupatse nzeru ndi kuzindikira.+ Akupatsenso lamulo lotsogolera Isiraeli, kuti usunge chilamulo cha Yehova Mulungu wako.+

  • Yobu 32:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndithudi, mzimu wa anthu

      Ndiponso mpweya wa Wamphamvuyonse n’zimene zimawachititsa kumvetsa zinthu.+

  • Salimo 119:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  35 Ndiyendetseni m’njira ya malamulo anu,+

      Pakuti ndikukondwera ndi njira imeneyi.+

  • Mlaliki 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Poti zonse zanenedwa, mfundo yaikulu ndi yakuti: Opa Mulungu woona+ ndi kusunga malamulo ake+ chifukwa zimenezi ndiye zimene munthu ayenera kuchita.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena