Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “Tsopano Aisiraeli inu, kodi Yehova Mulungu wanu akufuna kuti muzichita chiyani,+ koposa kuopa+ Yehova Mulungu wanu kuti muziyenda m’njira zake zonse,+ kukonda+ ndi kutumikira Yehova Mulungu wanu ndi mtima wanu wonse, ndi moyo wanu wonse,+

  • Yobu 28:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Ndiyeno anauza munthu kuti,

      ‘Tamvera, kuopa Yehova ndiko nzeru,+

      Ndipo kupatuka pa choipa ndiko kumvetsa zinthu.’”+

  • Salimo 111:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chiyambi cha nzeru ndicho kuopa Yehova.+

      ש [Sin]

      Onse otsatira malamulo a Mulungu ndi ozindikira.+

      ת [Taw]

      Iye ayenera kutamandidwa mpaka muyaya.+

  • Miyambo 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kuopa Yehova ndiko chiyambi cha kudziwa zinthu.+ Nzeru ndi malangizo zimanyozedwa ndi zitsiru.*+

  • Miyambo 8:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuopa Yehova kumatanthauza kudana ndi zoipa.+ Ndimadana ndi kudzikweza, kunyada,+ njira yoipa ndiponso pakamwa ponena zopotoka.+

  • Miyambo 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kuopa Yehova ndiko chiyambi cha nzeru.+ Kudziwa Woyera Koposa, ndiko kumvetsa zinthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena