Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 63:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Moyo wanga wakhutira ndi gawo labwino kwambiri, wakhutira ndi zinthu zabwino kwambiri,+

      Ndipo milomo yanga ikukutamandani ndi mfuu yachisangalalo.+

  • Salimo 71:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Inu Mulungu, mwandiphunzitsa kuyambira pa unyamata wanga,+

      Ndipo mpaka pano ndikunena za ntchito zanu zodabwitsa.+

  • Salimo 145:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo adzalankhula mosefukira za kuchuluka kwa ubwino wanu,+

      Ndipo adzafuula mokondwera chifukwa cha chilungamo chanu.+

  • Yohane 4:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Koma amene adzamwa madzi amene ine ndidzam’patse sadzamvanso ludzu m’pang’ono pomwe.+ Ndipo madzi amene ndidzam’patse, adzasanduka kasupe wa madzi+ otuluka mwa iye, opatsa moyo wosatha.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena