Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mapazi a okhulupirika ake amawateteza.+

      Koma anthu oipa amawawononga mu mdima,+

      Pakuti munthu sakhala wapamwamba chifukwa cha mphamvu zake.+

  • Salimo 91:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Iwo adzakunyamula m’manja mwawo,+

      Kuti phazi lako lisawombe mwala uliwonse.+

  • Miyambo 3:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Pakuti Yehova ndiye amene uzidzamudalira,+ ndipo adzateteza phazi lako kuti lisakodwe.+

  • Luka 1:79
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 79 ndipo kudzaunikira amene akhala mu mdima ndi mu mthunzi wa imfa,+ ndi kutsogolera bwinobwino mapazi athu panjira yamtendere.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena