Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 91:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pakuti adzalamula angelo ake za iwe,+

      Kuti akuteteze m’njira zako zonse.+

  • Salimo 97:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Inu okonda Yehova+ danani nacho choipa.+

      Iye amateteza moyo wa anthu ake okhulupirika.+

      Amawalanditsa m’manja mwa anthu oipa.+

  • Salimo 121:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Iye sangalole kuti phazi lako lipunthwe.+

      Amene amakuyang’anira sangawodzere.+

  • Miyambo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 mwa kuyang’anitsitsa njira zachiweruzo,+ ndipo adzateteza njira ya anthu ake okhulupirika.+

  • Luka 1:79
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 79 ndipo kudzaunikira amene akhala mu mdima ndi mu mthunzi wa imfa,+ ndi kutsogolera bwinobwino mapazi athu panjira yamtendere.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena