Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 56:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Ndikomereni mtima inu Mulungu wanga, chifukwa munthu wopanda pake akufuna kundiwakha ndi pakamwa pake.+

      Akulimbana nane tsiku lonse ndi kundipondereza.+

  • Salimo 76:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti mkwiyo wa munthu udzakutamandani,+

      Mkwiyo wake wotsala mudzaumangirira m’chiuno mwanu.

  • Miyambo 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tiye tikawameze amoyo+ ngati mmene amachitira Manda,*+ tikawameze athunthu ngati amene akupita kudzenje.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena