Deuteronomo 28:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Madalitso onsewa adzakutsata ndi kukupeza+ chifukwa ukumvera mawu a Yehova Mulungu wako: Salimo 147:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Iye akukhazikitsa mtendere m’dziko lako.+Ndipo akupitirizabe kukukhutiritsa ndi tirigu wabwino koposa.+
14 Iye akukhazikitsa mtendere m’dziko lako.+Ndipo akupitirizabe kukukhutiritsa ndi tirigu wabwino koposa.+