Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 1:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Pa chiyambi,+ Mulungu+ analenga+ kumwamba ndi dziko lapansi.+

  • Yobu 38:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndani anaika nzeru+ m’mitambo,

      Kapena zinthu zochitika kuthambo, ndani anazipatsa kuzindikira?+

  • Miyambo 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yehova anayala maziko a dziko lapansi mwanzeru.+ Anakhazikitsa kumwamba mozindikira.+

  • Yeremiya 10:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mulungu woona ndi amene anapanga dziko lapansi ndi mphamvu zake,+ amene mwanzeru zake+ anakhazikitsa dziko limene anthu amakhalamo. Iye ndi amenenso anayala kumwamba mwa kuzindikira kwake.+

  • Yeremiya 51:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mulungu woona ndi amene anapanga dziko lapansi ndi mphamvu zake,+ amene mwanzeru+ zake anakhazikitsa dziko+ limene anthu amakhalamo. Iye ndi amenenso anayala kumwamba mwa kuzindikira kwake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena