15 Chotero ndinapita kwa anthu otengedwa ukapolo amene anali ku Tele-abibu, amene anali kukhala+ pafupi ndi mtsinje wa Kebara.+ Ndinayamba kukhala pamalo pamene anthuwo anali kukhala ndipo ndinakhala pamenepo masiku 7. Ndinangokhala phee pakati pawo, ndili m’maganizo.+