Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mumandipatsa chakudya patebulo, pamaso pa anthu ondichitira zoipa.+

      Mwadzoza mutu wanga ndi mafuta.+

      Chikho changa ndi chodzaza bwino.+

  • Miyambo 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti lamulolo ndilo nyale,+ ndipo malangizo ndiwo kuwala,+ komanso kudzudzula* kowongola zolakwa ndiko njira yamoyo,+

  • Miyambo 19:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Menya wonyoza+ kuti wosadziwa zinthu achenjere.+ Ndipo womvetsa zinthu uyenera kum’dzudzula kuti adziwe zinthu zowonjezereka.+

  • Yakobo 5:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kodi pali wina amene akudwala pakati panu?+ Aitane akulu a mpingo,+ ndipo iwo amupempherere ndi kumupaka mafuta+ m’dzina la Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena