Salimo 31:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Koma ine chikhulupiriro changa chili mwa inu Yehova.+Ndipo ndikunena kuti: “Inu ndinu Mulungu wanga.”+ Yohane 20:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Yesu anati: “Usandikangamire. Pakuti sindinakwerebe kwa Atate. Koma pita kwa abale anga+ ukawauze kuti, ‘Ine ndikukwera kwa Atate+ wanga ndi Atate wanu, kwa Mulungu wanga+ ndi Mulungu wanu.’”+
14 Koma ine chikhulupiriro changa chili mwa inu Yehova.+Ndipo ndikunena kuti: “Inu ndinu Mulungu wanga.”+
17 Yesu anati: “Usandikangamire. Pakuti sindinakwerebe kwa Atate. Koma pita kwa abale anga+ ukawauze kuti, ‘Ine ndikukwera kwa Atate+ wanga ndi Atate wanu, kwa Mulungu wanga+ ndi Mulungu wanu.’”+