Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Yehova adzalamulira monga mfumu mpaka kalekale. Adzalamulira mpaka muyaya.+

  • Salimo 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova ndi Mfumu mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

      Mitundu yatheratu padziko lapansi.+

  • Salimo 145:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ufumu wanu ndi ufumu umene udzakhalapobe mpaka kalekale.+

      Ulamuliro wanu udzakhalapobe ku mibadwo yonse.+

  • Danieli 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ine ndikulamula+ kuti m’zigawo zonse za ufumu wanga, anthu azinjenjemera ndi kuchita mantha pamaso pa Mulungu wa Danieli.+ Pakuti iye ndi Mulungu wamoyo, amene adzakhalapo mpaka kalekale+ ndipo ufumu wake+ sudzawonongeka+ komanso ulamuliro wake udzakhalapo kwamuyaya.+

  • Chivumbulutso 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mngelo wa 7 analiza lipenga+ lake. Ndipo kumwamba kunamveka mawu osiyanasiyana, akunena mokweza kuti: “Ufumu wa dziko wakhala ufumu wa Ambuye wathu+ ndi wa Khristu wake.+ Iye adzalamulira monga mfumu kwamuyaya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena