Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova ndi Mfumu mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

      Mitundu yatheratu padziko lapansi.+

  • Salimo 146:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehova adzakhala mfumu mpaka kalekale,+

      Mulungu wako, iwe Ziyoni, adzakhala mfumu ku mibadwomibadwo.+

      Tamandani Ya, anthu inu!+

  • Danieli 4:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Zizindikiro zake n’zazikulu ndipo zodabwitsa zake n’zamphamvu.+ Ufumu wake udzakhalapo mpaka kalekale+ ndipo ulamuliro wake udzakhalapo ku mibadwomibadwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena