Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Yehova ndi Mfumu mpaka kalekale, ndithu mpaka muyaya.+

      Mitundu yatheratu padziko lapansi.+

  • Salimo 29:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Yehova wakhala pampando wake wachifumu pamwamba pa chigumula,*+

      Ndipo Yehova ndi mfumu mpaka kalekale.+

  • Salimo 66:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye akulamulira ndi mphamvu zake mpaka kalekale.+

      Maso ake akuyang’anitsitsa mitundu ya anthu.+

      Koma anthu oumitsa khosi asadzikweze.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 90:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mapiri asanabadwe,+

      Kapena musanakhazikitse dziko lapansi+ ndi malo okhalapo anthu,*+

      Inu ndinu Mulungu kuyambira kalekale mpaka kalekale.+

  • Yeremiya 10:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma Yehova ndi Mulungu woonadi.+ Iye ndi Mulungu wamoyo+ ndipo ndi Mfumu mpaka kalekale.+ Dziko lapansi lidzagwedezeka ndi mkwiyo wake,+ ndipo palibe mitundu ya anthu imene idzalimbe pamene iye akuidzudzula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena