Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 21:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Ndipo izi ndizo zigamulo zoti uwaikire:+

  • Numeri 15:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Pambuyo pake Yehova anauza Mose kuti: “Munthuyo aphedwe basi!+ Khamu lonselo likam’ponye miyala kunja kwa msasa.”+

  • Nehemiya 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno munatsikira paphiri la Sinai+ ndi kulankhula nawo muli kumwamba.+ Munawapatsa zigamulo zowongoka+ ndi malamulo a choonadi,+ mfundo zabwino ndi malangizo abwino.+

  • Salimo 119:137
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 137 Ndinu wolungama inu Yehova,+

      Ndipo zigamulo zanu ndi zowongoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena