Salimo 92:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndipo ndidzatero pogwiritsa ntchito choimbira cha zingwe 10 ndi choimbira cha zingwe zitatu.+Ndidzaimba nyimbo yomveka bwino ndi zeze.+ Salimo 144:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Inu Mulungu, ine ndidzakuimbirani nyimbo yatsopano.+Ndidzaimba nyimbo yokutamandani ndi choimbira cha zingwe 10.+ Yesaya 38:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Inu Yehova bwerani mudzandipulumutse,+ ndipo tidzaimba nyimbo zimene ine ndinapeka. Ndidzaimba ndi zoimbira za zingwe+Kunyumba ya Yehova masiku onse a moyo wathu.’”+
3 Ndipo ndidzatero pogwiritsa ntchito choimbira cha zingwe 10 ndi choimbira cha zingwe zitatu.+Ndidzaimba nyimbo yomveka bwino ndi zeze.+
9 Inu Mulungu, ine ndidzakuimbirani nyimbo yatsopano.+Ndidzaimba nyimbo yokutamandani ndi choimbira cha zingwe 10.+ Yesaya 38:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Inu Yehova bwerani mudzandipulumutse,+ ndipo tidzaimba nyimbo zimene ine ndinapeka. Ndidzaimba ndi zoimbira za zingwe+Kunyumba ya Yehova masiku onse a moyo wathu.’”+
20 Inu Yehova bwerani mudzandipulumutse,+ ndipo tidzaimba nyimbo zimene ine ndinapeka. Ndidzaimba ndi zoimbira za zingwe+Kunyumba ya Yehova masiku onse a moyo wathu.’”+