Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 51:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mundisambitse bwinobwino ndi kuchotsa cholakwa changa,+

      Ndiyeretseni ku tchimo langa.+

  • Salimo 73:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndithudi, ndayeretsa mtima wanga pachabe,+

      Ndipo ndasamba m’manja mwanga pachabe posonyeza kuti ndine wopanda cholakwa.+

  • Yesaya 1:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Sambani,+ dziyeretseni.+ Chotsani zochita zanu zoipa pamaso panga.+ Lekani kuchita zoipa.+

  • Mateyu 27:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Poona kuti sizikuthandiza, komanso pakuyambika chipolowe, Pilato anangotenga madzi+ ndi kusamba m’manja pamaso pa khamu la anthulo, n’kunena kuti: “Inetu ndasamba m’manja, ndilibe mlandu wa magazi a munthu uyu. Zonse zili kwa inu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena