Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 69:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Ndipo ine mtumiki wanu musandibisire nkhope yanu.+

      Ndiyankheni mwamsanga, chifukwa ndasautsika kwambiri.+

  • Salimo 143:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Fulumirani, ndiyankheni inu Yehova.+

      Mphamvu zanga zatha.+

      Musandibisire nkhope yanu,+

      Chifukwa mukatero ndikhala ngati anthu amene akutsikira kudzenje la manda.+

  • Yesaya 59:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Ayi si choncho. Koma zolakwa za anthu inu n’zimene zakulekanitsani ndi Mulungu wanu,+ ndipo machimo anu amuchititsa kuti akubisireni nkhope yake, kuti asamve zimene mukunena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena