Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti simudzasiya moyo wanga m’Manda.+

      Simudzalola kuti wokhulupirika wanu aone dzenje.+

  • Salimo 86:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pakuti kukoma mtima kosatha kumene mwandisonyeza ndi kwakukulu,+

      Ndipo mwapulumutsa moyo wanga ku Manda, kumalo apansi penipeni.+

  • Machitidwe 2:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Choncho pokhala mneneri, iye anaoneratu zapatsogolo ndi kuneneratu za kuuka kwa Khristu. Ananeneratu kuti iye sanasiyidwe m’Manda, komanso kuti thupi lake silinavunde.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena