Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zikanakhala bwino mukanandibisa m’Manda,+

      Mukanandibisa mpaka mkwiyo wanu utachoka,

      Mukanati mundiikire nthawi+ n’kudzandikumbukira.+

  • Yobu 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndidzaitana dzenje+ kuti, ‘Ndinu bambo anga!’

      Kwa mphutsi+ ndidzati, ‘Mayi anga ndi mlongo wanga!’

  • Yesaya 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 M’malo mopeza mtendere ndinapeza zowawa, zowawatu zedi!+

      Inuyo mwamamatira moyo wanga ndipo mwauteteza kuti usapite kudzenje la chiwonongeko.+

      Pakuti machimo anga onse mwawaponyera kumbuyo kwanu.+

  • Machitidwe 13:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Ndipo mu salimo lina akunenanso kuti, ‘Simudzalola kuti thupi la wokhulupirika wanu livunde.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena