Salimo 28:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Ndikuitana inu Yehova.+Inu Thanthwe langa, musatseke makutu anu pamene ine ndikuitana,+Kuti musakhale chete pamaso panga,+Kutinso ine ndisafanane ndi amene akutsikira kudzenje la manda.+ Salimo 30:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Inu Yehova, mwanditulutsa m’Manda,+Mwandisunga ndi moyo, kuti ndisatsikire m’dzenje.+ Salimo 86:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Pakuti kukoma mtima kosatha kumene mwandisonyeza ndi kwakukulu,+Ndipo mwapulumutsa moyo wanga ku Manda, kumalo apansi penipeni.+ Salimo 88:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Ndakhala womasuka ngati anthu akufa,+Ngati anthu ophedwa amene agona m’manda,+Anthu amene simukuwakumbukiransoKomanso amene sakulandira thandizo kuchokera m’manja mwanu.+ Yona 2:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Ndinatsikira m’tsinde mwenimweni mwa mapiri.Zotsekera za dziko lapansi zinanditsekereza kuti ndikhale komweko mpaka kalekale.*Koma inu Yehova Mulungu wanga, munanditulutsa m’dzenje ndili wamoyo.+
28 Ndikuitana inu Yehova.+Inu Thanthwe langa, musatseke makutu anu pamene ine ndikuitana,+Kuti musakhale chete pamaso panga,+Kutinso ine ndisafanane ndi amene akutsikira kudzenje la manda.+
13 Pakuti kukoma mtima kosatha kumene mwandisonyeza ndi kwakukulu,+Ndipo mwapulumutsa moyo wanga ku Manda, kumalo apansi penipeni.+
5 Ndakhala womasuka ngati anthu akufa,+Ngati anthu ophedwa amene agona m’manda,+Anthu amene simukuwakumbukiransoKomanso amene sakulandira thandizo kuchokera m’manja mwanu.+
6 Ndinatsikira m’tsinde mwenimweni mwa mapiri.Zotsekera za dziko lapansi zinanditsekereza kuti ndikhale komweko mpaka kalekale.*Koma inu Yehova Mulungu wanga, munanditulutsa m’dzenje ndili wamoyo.+