Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 33:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mulungu amasangalatsidwa naye ndi kunena kuti,

      ‘M’pulumutseni kuti asapite m’dzenje,+

      Chifukwa ndapeza dipo.*+

  • Salimo 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti simudzasiya moyo wanga m’Manda.+

      Simudzalola kuti wokhulupirika wanu aone dzenje.+

  • Salimo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, mwanditulutsa m’Manda,+

      Mwandisunga ndi moyo, kuti ndisatsikire m’dzenje.+

  • Yesaya 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 M’malo mopeza mtendere ndinapeza zowawa, zowawatu zedi!+

      Inuyo mwamamatira moyo wanga ndipo mwauteteza kuti usapite kudzenje la chiwonongeko.+

      Pakuti machimo anga onse mwawaponyera kumbuyo kwanu.+

  • Machitidwe 2:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Choncho pokhala mneneri, iye anaoneratu zapatsogolo ndi kuneneratu za kuuka kwa Khristu. Ananeneratu kuti iye sanasiyidwe m’Manda, komanso kuti thupi lake silinavunde.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena