Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 33:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Iye wandiwombola kuti ndisapite kudzenje,+

      Ndipo moyo wanga udzaona kuwala.’

  • Salimo 30:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kodi magazi anga angakhale ndi phindu lanji ngati nditatsikira kudzenje la manda?+

      Kodi fumbi lidzakutamandani?+ Kodi lidzalengeza kuti inu ndinu woona?+

  • Salimo 69:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Musalole kuti mtsinje wa madzi othamanga undikokolole,+

      Kapena kuti madzi akuya andimize,

      Kapenanso kuti dzenje* lindimeze ndi kutseka pakamwa pake.+

  • Yesaya 38:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti Manda sangakutamandeni.+ Imfa singakulemekezeni.+

      Anthu amene akutsikira kudzenje sangayembekezere kukhulupirika kwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena