Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 30:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kodi magazi anga angakhale ndi phindu lanji ngati nditatsikira kudzenje la manda?+

      Kodi fumbi lidzakutamandani?+ Kodi lidzalengeza kuti inu ndinu woona?+

  • Salimo 88:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kodi anthu akufa mudzawachitira zodabwitsa?+

      Kapena kodi anthu akufa, anthu amene sangachite kanthu, adzauka?+

      Kodi adzakutamandani?+ [Seʹlah.]

  • Salimo 146:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mzimu* wake umachoka,+ ndipo iye amabwerera kunthaka.+

      Pa tsiku limenelo zonse zimene anali kuganiza zimatheratu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena