Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma mwamuna wamphamvu amafa ndipo amagona pansi atagonjetsedwa.

      Munthu wochokera kufumbi amatha. Kodi ali kuti?+

  • Yobu 17:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Masiku anga atha,+ zolinga zanga zasokonezedwa,+

      Zofuna za mtima wanga zasokonezedwa.

  • Mlaliki 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa,+ koma akufa sadziwa chilichonse.+ Iwo salandiranso malipiro alionse, chifukwa zonse zimene anthu akanawakumbukira nazo zaiwalika.+

  • Mlaliki 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chilichonse chimene dzanja lako lapeza kuti lichite, uchichite ndi mphamvu zako zonse,+ pakuti kulibe kugwira ntchito, kuganiza zochita, kudziwa zinthu,+ kapena nzeru,+ ku Manda*+ kumene ukupitako.+

  • Yesaya 38:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti Manda sangakutamandeni.+ Imfa singakulemekezeni.+

      Anthu amene akutsikira kudzenje sangayembekezere kukhulupirika kwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena