Genesis 37:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Ana ake onse aamuna ndi aakazi anali kupita kukam’tonthoza,+ koma iye anali kukana kutonthozedwa. Anali kunena kuti:+ “Ayi! Ndidzalira mpaka kutsikira ku Manda* kumene kuli mwana wanga.” Ndipo bambo akewo anapitiriza kumulira. 1 Mafumu 2:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Iweyo uchite zinthu monga mwa nzeru zako,+ ndipo usalole kuti imvi zake zitsikire ku Manda*+ mwamtendere.+ Yesaya 5:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Choncho, Manda* akulitsa malo ake ndipo atsegula kwambiri pakamwa pake kupitirira malire.+ Anthu olemekezeka a mumzindawo, khamu lake, phokoso lake ndi chikondwerero chake zidzatsikira m’mandamo.+
35 Ana ake onse aamuna ndi aakazi anali kupita kukam’tonthoza,+ koma iye anali kukana kutonthozedwa. Anali kunena kuti:+ “Ayi! Ndidzalira mpaka kutsikira ku Manda* kumene kuli mwana wanga.” Ndipo bambo akewo anapitiriza kumulira.
6 Iweyo uchite zinthu monga mwa nzeru zako,+ ndipo usalole kuti imvi zake zitsikire ku Manda*+ mwamtendere.+
14 Choncho, Manda* akulitsa malo ake ndipo atsegula kwambiri pakamwa pake kupitirira malire.+ Anthu olemekezeka a mumzindawo, khamu lake, phokoso lake ndi chikondwerero chake zidzatsikira m’mandamo.+