Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Iye amene moyo+ wa aliyense uli m’dzanja lake,

      Ndiponso mzimu wa anthu onse.+

  • Salimo 104:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mukaphimba nkhope yanu, zimasokonezeka.+

      Mukachotsa mzimu wawo, zimafa,+

      Ndipo zimabwerera kufumbi.+

  • Mlaliki 8:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Palibe munthu amene ali ndi mphamvu pa mzimu kuti auletse mzimuwo.+ Palibenso amene ali ndi mphamvu pa tsiku la imfa.+ Palibe amene samenya nawo nkhondo,+ ndipo kuchita zoipa sikudzapulumutsa amene amachita zoipawo.+

  • Mateyu 27:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Pamenepo Yesu anafuulanso mokweza mawu, kenako anatsirizika.+

  • Machitidwe 7:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Iwo anapitiriza kumuponya miyala Sitefano, pamene iye anali kuchonderera kuti: “Ambuye Yesu, landirani mzimu* wanga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena