Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Anthu oipa+ adzapita ku Manda,+

      Ngakhalenso anthu onse a mitundu ina amene aiwala Mulungu.+

  • Salimo 52:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu adzakupasula kosatha.+

      Adzakugwetsa ndi kukukokera kunja kwa hema wako,+

      Ndipo adzakuzula ndithu m’dziko la anthu amoyo.+ [Seʹlah.]

  • Miyambo 14:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Woipa adzakankhidwa chifukwa cha kuipa kwake,+ koma wolungama adzapeza malo othawirako chifukwa cha mtima wake wosagawanika.+

  • Yesaya 28:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pangano lanu limene mwachita ndi Imfa lidzatha,+ ndipo masomphenya anu amene mwaona ndi Manda sadzagwira ntchito.+ Madzi osefukira akadzadutsa+ adzakukokololani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena