Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, mwanditulutsa m’Manda,+

      Mwandisunga ndi moyo, kuti ndisatsikire m’dzenje.+

  • Salimo 49:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Kuti akhale ndi moyo mpaka muyaya osaona dzenje la manda.+

  • Salimo 143:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Fulumirani, ndiyankheni inu Yehova.+

      Mphamvu zanga zatha.+

      Musandibisire nkhope yanu,+

      Chifukwa mukatero ndikhala ngati anthu amene akutsikira kudzenje la manda.+

  • Miyambo 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tiye tikawameze amoyo+ ngati mmene amachitira Manda,*+ tikawameze athunthu ngati amene akupita kudzenje.+

  • Yesaya 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Koma adzakutsitsira ku Manda,+ pansi penipeni pa dzenje.+

  • Yona 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndinatsikira m’tsinde mwenimweni mwa mapiri.

      Zotsekera za dziko lapansi zinanditsekereza kuti ndikhale komweko mpaka kalekale.*

      Koma inu Yehova Mulungu wanga, munanditulutsa m’dzenje ndili wamoyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena