Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mapazi a okhulupirika ake amawateteza.+

      Koma anthu oipa amawawononga mu mdima,+

      Pakuti munthu sakhala wapamwamba chifukwa cha mphamvu zake.+

  • Salimo 115:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Akufa satamanda Ya,+

      Ngakhalenso aliyense wotsikira kuli chete.+

  • Mlaliki 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pakuti amoyo amadziwa kuti adzafa,+ koma akufa sadziwa chilichonse.+ Iwo salandiranso malipiro alionse, chifukwa zonse zimene anthu akanawakumbukira nazo zaiwalika.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena