Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 50:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Nthawi zonse ukaona wakuba unali kusangalala naye.+

      Ndipo unali kugwirizana ndi anthu achigololo.+

  • Hoseya 7:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iwo amasangalatsa mfumu ndi zoipa zawo, ndiponso amasangalatsa akalonga ndi chinyengo chawo.+

  • Luka 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Iwo anakondwa, ndipo anagwirizana kuti amupatse ndalama zasiliva.+

  • Aroma 1:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Amenewa ngakhale kuti amalidziwa bwino lamulo lolungama la Mulungu,+ lakuti amene amachita zinthu zimenezi n’ngoyenera imfa,+ iwo amapitiriza kuzichita. Kuwonjezera apo, amagwirizananso+ ndi anthu amene amachita zimenezo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena