Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 19:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 “Usasunthe zizindikiro za malire a mnzako,+ makolo anu ataika kale malire a cholowa chimene udzalandira, m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa kuti ulitenge kukhala lako.

  • Deuteronomo 27:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “‘Wotembereredwa ndi munthu wosuntha chizindikiro cha malire a mnzake.’+ (Anthu onse ayankhe kuti, ‘Zikhale momwemo!’)

  • Yobu 24:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Pali anthu amene amasuntha malire,+

      Iwo alanda gulu la ziweto kuti aziziweta.

  • Hoseya 5:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Akalonga a Yuda akhala ngati anthu osuntha malire.+ Ndidzawakhuthulira mkwiyo wanga ngati madzi.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena