Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Rute 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Maso ako akhale pamunda umene akukolola, ndipo uzipita nawo limodzi kumeneko. Anyamatawa ndawalamula kuti asakukhudze.+ Ukamva ludzu, nawenso uzipita kumitsuko kukamwa madzi amene anyamatawa azitunga.”+

  • 2 Samueli 23:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Patapita nthawi, Davide anafotokoza zimene anali kulakalaka kuti: “Ndikanakonda ndikanamwa madzi a m’chitsime cha ku Betelehemu chimene chili pachipata!”+

  • Mateyu 10:42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 42 Aliyense wopatsa mmodzi wa tiana iti ngakhale madzi ozizira okha m’kapu kuti amwe chifukwa ndi wophunzira, ndithu ndikukuuzani, ameneyo mphoto yake sidzatayika ngakhale pang’ono.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena