Genesis 3:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Pambuyo pake, iwo anamva mawu a Yehova Mulungu pamene iye anali kuyendayenda m’mundamo pa nthawi ya kamphepo kayeziyezi.+ Mwamuna ndi mkaziyo atamva, anathawa n’kukabisala pakati pa mitengo ya m’mundamo kuti Yehova Mulungu asawaone.+ 1 Samueli 15:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Poyankha Sauli anati: “Anthuwa+ azitenga kwa Aamaleki, chifukwa sanaphe nkhosa ndi ng’ombe zabwino kwambirizi n’cholinga chofuna kuzipereka nsembe kwa Yehova Mulungu wanu.+ Koma zina zonse zotsala taziwononga.” Salimo 32:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pamene ndinakhala chete osaulula machimo anga, mafupa anga anafooka, chifukwa tsiku lonse ndinali kuvutika mumtima mwanga.+
8 Pambuyo pake, iwo anamva mawu a Yehova Mulungu pamene iye anali kuyendayenda m’mundamo pa nthawi ya kamphepo kayeziyezi.+ Mwamuna ndi mkaziyo atamva, anathawa n’kukabisala pakati pa mitengo ya m’mundamo kuti Yehova Mulungu asawaone.+
15 Poyankha Sauli anati: “Anthuwa+ azitenga kwa Aamaleki, chifukwa sanaphe nkhosa ndi ng’ombe zabwino kwambirizi n’cholinga chofuna kuzipereka nsembe kwa Yehova Mulungu wanu.+ Koma zina zonse zotsala taziwononga.”
3 Pamene ndinakhala chete osaulula machimo anga, mafupa anga anafooka, chifukwa tsiku lonse ndinali kuvutika mumtima mwanga.+