Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 11:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndipo Mose ndi Aroni anachita zozizwitsa zonsezi pamaso pa Farao.+ Koma Yehova analola Farao kuumitsa mtima wake, moti sanalole ana a Isiraeli kuchoka m’dziko lake.+

  • 2 Mbiri 36:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kuwonjezera pamenepo, Zedekiya anapandukira Mfumu Nebukadinezara+ yomwe inali itamulumbiritsa kwa Mulungu,+ ndipo anapitiriza kuumitsa khosi lake ndi mtima wake+ kuti asabwerere kwa Yehova Mulungu wa Isiraeli.

  • Salimo 75:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Musakweze nyanga yanu pamwamba.

      Musalankhule modzikuza.+

  • Yeremiya 17:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma iwo sanamvere kapena kutchera khutu+ moti anapitiriza kuumitsa khosi+ lawo kuti asamve ndi kulandira mwambo.”’*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena