Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 34:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iye anachita zoyenera pamaso pa Yehova+ ndipo anayenda m’njira za Davide kholo lake.+ Sanapatukire mbali ya kudzanja lamanja kapena lamanzere.+

  • Salimo 44:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Zonsezi ndi zimene zatigwera, koma sitinakuiwaleni,+

      Sitinachite mwachinyengo ndi pangano lanu.+

  • Miyambo 3:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mwana wanga, usaiwale lamulo langa,+ ndipo mtima wako usunge malamulo anga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena