Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Koma nkhungu+ inali kukwera m’mwamba kuchokera padziko lapansi, ndipo inali kunyowetsa nthaka yonse.+

  • Genesis 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 M’chaka cha 600 cha moyo wa Nowa, m’mwezi wachiwiri,* pa tsiku la 17 la mweziwo, pa tsiku limeneli akasupe onse amadzi akuya* anaphulika ndipo zotsekera madzi akumwamba zinatseguka.+

  • Genesis 8:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Pamenepo, akasupe a madzi akuya+ ndi zotsekera madzi+ akumwamba zinatsekeka, choncho madzi omwe anali kukhuthuka kuchokera kumwamba anasiya.

  • Salimo 104:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Munalikuta ndi madzi ngati mwalikuta ndi nsalu.+

      Madziwo anakwera kupitirira mapiri.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena