Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndithudi, madalitso amene Mulungu amapereka ndi ochuluka kwambiri.+ Nzeru+ zake n’zozama, ndiponso iye ndi wodziwa zinthu kwambiri.+ Ziweruzo zake ndi zosasanthulika,+ ndipo ndani angatulukire njira zake?

  • Aroma 16:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Kwa Mulungu wanzeru yekhayo,+ kukhale ulemerero+ kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu.+ Ame.

  • 1 Akorinto 1:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kodi wanzeru ali kuti? Mlembi ali kuti?+ Katswiri wa mtsutso+ wa nthawi* ino ali kuti?+ Kodi Mulungu sanapange nzeru za dzikoli kukhala zopusa?+

  • 1 Akorinto 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 kuti chikhulupiriro chanu chisazikike pa nzeru za anthu,+ koma pa mphamvu ya Mulungu.+

  • Aefeso 3:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zinakhala choncho kuti maboma ndi maulamuliro+ amene ali m’malo akumwamba adziwe tsopano mbali zambirimbiri za nzeru ya Mulungu+ kudzera mwa mpingo.+

  • Yakobo 3:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma nzeru+ yochokera kumwamba, choyamba, ndi yoyera,+ kenako yamtendere,+ yololera,+ yokonzeka kumvera, yodzaza ndi chifundo ndi zipatso zabwino,+ yopanda tsankho,+ ndiponso yopanda chinyengo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena